Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 2:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ndipo mlongo wake wa mwanayo adaimirira pafupi namangopenyetsetsa, kuti aone zimene zimchitikire mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mlongo wake wa mwanayo anayima pataliko kuti aone chimene chidzamuchitikira mwanayo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 2:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Miriyamu mneneriyo, mlongo wa Aroni, anagwira lingaka m'dzanja lake; ndipo akazi onse anatuluka kumtsata ndi malingaka ndi kuthira mang'ombe.


Pakuti ndinakukwezani kukutulutsani m'dziko la Ejipito, ndi kuombola inu m'nyumba ya ukapolo; ndipo ndinatuma akutsogolereni Mose, Aroni, ndi Miriyamu.


Ndipo ana a Israele, ndilo khamu lonse, analowa m'chipululu cha Zini mwezi woyamba; ndipo anthu anakhala mu Kadesi; kumeneko anafa Miriyamu, naikidwa komweko.


Ndipo dzina lake la mkazi wake wa Amuramu ndiye Yokebede, mwana wamkazi wa Levi, wobadwira Levi mu Ejipito; ndipo iye anambalira Amuramu, Aroni ndi Mose, ndi Miriyamu mlongo wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa