Eksodo 2:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndipo mlongo wake wa mwanayo adaimirira pafupi namangopenyetsetsa, kuti aone zimene zimchitikire mwanayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mlongo wake wa mwanayo anayima pataliko kuti aone chimene chidzamuchitikira mwanayo. Onani mutuwo |