Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 5:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo ndinati kwa mthenga wakulankhula ndi ine, Amenewa amuka naye kuti efayo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo ndinati kwa mthenga wakulankhula ndi ine, Amenewa amuka naye kuti efayo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono ndidafunsa mngelo amene ankalankhula nane kuti, “Nanganso gondololi akupita nalo kuti?” Iye adandiyankha kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ine ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane kuti, “Dengulo akupita nalo kuti?”

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 5:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinati, Upita kuti? Ndipo anati kwa ine, Kukayesa Yerusalemu, kuona ngati chitando chake nchotani, ndi m'litali mwake motani.


Ndipo anati kwa ine, Kummangira nyumba m'dziko la Sinara; kuti amuike efayo, namkhazikeko pamalo kwake.


Pamenepo ndinakweza maso anga, ndinapenya, ndipo taonani, anatuluka akazi awiri, ndi m'mapiko mwao munali mphepo; ndipo anali nao mapiko ngati mapiko a chumba, nanyamula efayo pakati padziko ndi thambo.


Ndipo ndinayankha ndinati kwa mthenga wolankhula ndi ine, Izi nziyani, mbuyanga?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa