Zekariya 5:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anati kwa ine, Kummangira nyumba m'dziko la Sinara; kuti amuike efayo, namkhazikeko pamalo kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anati kwa ine, Kummangira nyumba m'dziko la Sinara; kuti amuike efayo, namkhazikeko pa malo kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Akupita nalo ku dziko la Sinara kuti akalimangire nyumba. Nyumbayo ikadzatha, adzakhazikamo gondololo pa phaka lake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anayankha kuti, “Ku dziko la Babuloni kuti akalimangire nyumba. Nyumbayo ikadzatha, adzayikamo dengulo.” Onani mutuwo |