Zekariya 10:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ndidzawalimbitsa mwa Yehova; ndipo adzayendayenda m'dzina lake; ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ndidzawalimbitsa mwa Yehova; ndipo adzayendayenda m'dzina lake; ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ineyo ndidzalimbitsa anthu anga, ndipo adzakhala onyadira dzina la Chauta.” Ndikutero Ine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndidzalimbitsa iwo mwa Yehova ndipo adzayenda mʼdzina lake,” akutero Yehova. Onani mutuwo |