Zekariya 10:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo adzapita pakati pa nyanja ya nsautso, nadzapanda mafunde a m'nyanja, ndi maiwe onse a mtsinje adzaphwa; ndi kudzikuza kwa Asiriya kudzagwetsedwa; ndi ndodo yachifumu ya Ejipito idzachoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo adzapita pakati pa nyanja ya nsautso, nadzapanda mafunde a m'nyanja, ndi maiwe onse a mtsinje adzaphwa; ndi kudzikuza kwa Asiriya kudzagwetsedwa; ndi ndodo yachifumu ya Ejipito idzachoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pamene azidzaoloka nyanja ya ku Ejipito, ndidzathetsa mafunde a pa nyanjayo, madzi onse a mtsinje wa Nailo adzaphweratu. Kudzikuza kwa Asiriya kudzatha, ndipo ndodo yaufumu ya Ejipito idzathyoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Adzawoloka nyanja ya masautso; nyanja yokokoma idzagonja ndipo madzi onse a mu Nailo adzaphwa. Kudzikuza kwa Asiriya kudzatha ndipo ndodo yaufumu ya Igupto idzathyoka. Onani mutuwo |