Zekariya 10:10 - Buku Lopatulika10 Ndidzawatenganso kudziko la Ejipito, ndi kuwasonkhanitsa mu Asiriya; ndipo ndidzalowa nao m'dziko la Giliyadi ndi Lebanoni; koma sadzawafikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndidzawatenganso kudziko la Ejipito, ndi kuwasonkhanitsa m'Asiriya; ndipo ndidzalowa nao m'dziko la Giliyadi ndi Lebanoni; koma sadzawafikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndidzaŵatulutsa ku Ejipito ndi kupita nawo kwao, ndipo ndidzaŵasonkhanitsa kuchokera ku Asiriya. Ndidzaŵafikitsa ku dziko la Giliyadi ndi la Lebanoni mpaka kudzaza dziko lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndidzawabweretsa kuchokera ku Igupto ndipo ndidzawasonkhanitsa kuchokera ku Asiriya. Ndidzawabwezera ku Giliyadi ndi ku Lebanoni, mpaka malo woti nʼkukhalamo adzatheratu. Onani mutuwo |