Zekariya 10:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ndidzawafesa mwa mitundu ya anthu, ndipo adzandikumbukira m'maiko akutali; nadzakhala pamodzi ndi ana ao, nadzabwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ndidzawafesa mwa mitundu ya anthu, ndipo adzandikumbukira m'maiko akutali; nadzakhala pamodzi ndi ana ao, nadzabwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ngakhale ndidaŵabalalitsira pakati pa mitundu ya anthu, komabe ku maiko akutaliwo adzandikumbukira. Iwowo pamodzi ndi ana ao adzakhala moyo nadzabwerera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndinawamwaza pakati pa mitundu ina ya anthu, koma ku mayiko akutaliwo adzandikumbukira. Iwo pamodzi ndi ana awo adzapulumuka, ndipo adzabwerera. Onani mutuwo |