Zekariya 10:8 - Buku Lopatulika8 Ndidzawaimbira mluzu ndi kuwasonkhanitsa, pakuti ndawaombola; ndipo adzachuluka monga anachulukira kale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndidzawaimbira mluzu ndi kuwasonkhanitsa, pakuti ndawaombola; ndipo adzachuluka monga anachulukira kale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Ndidzaliza mluzu kuti anthu anga asonkhane pamodzi. Ndidaŵapulumutsa, ndipo adzachuluka monga momwe adaaliri masiku amakedzana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndidzaliza mluzu ndi kuwasonkhanitsa pamodzi. Ndithu ndawawombola; adzachulukana ngati poyamba paja. Onani mutuwo |