Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 5:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo ana a Israele anachita chotero, nawatulutsira kunja kwa chigono; monga Yehova adanena ndi Mose momwemo ana a Israele anachita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo ana a Israele anachita chotero, nawatulutsira kunja kwa chigono; monga Yehova adanena ndi Mose momwemo ana a Israele anachita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Aisraele adachitadi zimenezi, ndipo adaŵatulutsira kunja anthuwo. Ankachitadi monga momwe Chauta adaauzira Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Aisraeli anachitadi zimenezi. Anawatulutsira kunja kwa msasa monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu Uziya anali wakhate mpaka tsiku la imfa yake, nakhala m'nyumba ya padera, popeza ndiye wakhate; pakuti anadulidwa kunyumba ya Yehova; ndi Yotamu mwana wake anayang'anira nyumba ya mfumu naweruza anthu a m'dziko.


Ndipo anthu anawerama, nalambira. Ndipo ana a Israele anamuka nachita monga Yehova adalamulira Mose ndi Aroni; anachita momwemo.


Ndipo ana onse a Israele anachita monga Yehova adawalamulira Mose ndi Aroni, momwemo anachita.


muwatulutse amuna ndi akazi muwatulutsire kunja kwa chigono, kuti angadetse chigono chao, chimene ndikhala m'kati mwakemo.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa