Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 5:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:5
3 Mawu Ofanana  

Munthu akachita mosakhulupirika, nakachimwa osati dala, pa zopatulika za Yehova, azidza nayo nsembe yake yopalamula kwa Yehova, ndiyo nkhosa yamphongo yopanda chilema, ya m'gulu lake, monga umayesa mtengo wake potchula masekeli a siliva, kunena sekeli wa malo opatulika, ikhale nsembe yopalamula;


Ndipo ana a Israele anachita chotero, nawatulutsira kunja kwa chigono; monga Yehova adanena ndi Mose momwemo ana a Israele anachita.


Nena ndi ana a Israele, ndi kuti Mwamuna kapena mkazi akachita tchimo lililonse amachita anthu, kuchita mosakhulupirika pa Yehova, nakapalamuladi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa