Numeri 4:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ayale pa izi nsalu yofiira, ndi kuliphimba ndi chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kupisako mphiko zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ayale pa izi nsalu yofiira, ndi kuliphimba ndi chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kupisako mphiko zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono pamwamba pa zimenezo ayalepo nsalu yofiira, ndi kuziphimba zonsezo ndi zikopa zambuzi, ndipo apise mphiko m'zigwinjiri zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsono pamwamba pa izi aziyalapo nsalu yofiira, ndi kuzikuta mʼzikopa za akatumbu ndi kuyika mitengo yonyamulira mʼmalo mwake. Onani mutuwo |