Numeri 4:44 - Buku Lopatulika44 owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Chiŵerengero chao chidakwanira 3,200 potsata mabanja ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 3,200. Onani mutuwo |