Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 4:44 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 3,200.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

44 owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Chiŵerengero chao chidakwanira 3,200 potsata mabanja ao.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:44
7 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha amuna onse kuyambira a mwezi umodzi kapena kupitirirapo chinali 6,200.


Amuna onse kuyambira zaka makumi atatu mpaka makumi asanu amene anabwera kudzatumikira ntchito mu tenti ya msonkhano,


Ichi ndicho chinali chiwerengero cha mabanja a Amerari. Mose ndi Aaroni anawawerenga monga momwe Yehova anawalamulira kudzera mwa Mose.


Palibe mayesero amene mwakumana nawo oposa amene anthu ena onse anakumana nawo. Mulungu ngokhulupirika; sadzalola kuti inu muyesedwe koposa muyeso umene mutha kupirira. Koma pamene mwayesedwa, Iyenso adzakupatsani njira yopambanira mayeserowo.


Zotsekera za zipata zako zidzakhala za chitsulo ndi za mkuwa, ndi mphamvu zako zidzakhala ngati masiku a moyo wako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa