Numeri 34:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo malirewo adzatuluka kunka ku Zifuroni, ndi kutuluka kwake kudzakhala ku Hazara-Enani; ndiwo malire anu a kumpoto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo malirewo adzatuluka kunka ku Zifuroni, ndi kutuluka kwake kudzakhala ku Hazara-Enani; ndiwo malire anu a kumpoto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono malirewo afike mpaka ku Zifuroni, ndipo mathero ake akhale ku Hazarenani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 ndi kupitirira mpaka ku Ziforoni ndi kukathera ku Hazari-Enani. Awa ndiwo adzakhale malire anu a kumpoto. Onani mutuwo |