Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 34:23 - Buku Lopatulika

23 Wa ana a Yosefe; wa fuko la ana a Manase, kalonga Haniyele mwana wa Efodi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Wa ana a Yosefe; wa fuko la ana a Manase, kalonga Haniyele mwana wa Efodi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mwa ana a Yosefe, m'fuko la ana a Manase akhale Haniyele mwana wa Efodi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Hanieli mwana wa Efodi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Manase, mwana wa Yosefe;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 34:23
2 Mawu Ofanana  

Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.


Wa fuko la ana a Efuremu, kalonga Kemuwele mwana wa Sifutani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa