Numeri 34:22 - Buku Lopatulika22 Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 M'fuko la ana a Dani akhale Buki mwana wa Yogili. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Buki mwana wa Yogili, mtsogoleri wochokera ku fuko la Dani; Onani mutuwo |