Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 34:21 - Buku Lopatulika

21 Wa fuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Wa fuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 M'fuko la Benjamini akhale Elidadi mwana wa Kisiloni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Elidadi mwana wa Kisiloni, wochokera ku fuko la Benjamini;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 34:21
4 Mawu Ofanana  

Benjamini ndiye mmbulu wakulusalusa; m'mamawa adzadya chomotola, madzulo adzagawa zofunkha.


Apo pali Benjamini wamng'ono, wakuwachita ufumu, akulu a Yuda, ndi a upo wao, akulu a Zebuloni, akulu a Nafutali.


Wa fuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.


Za Benjamini anati, Wokondedwa wa Yehova adzakhala ndi Iye mokhazikika; am'phimba tsiku lonse, inde akhalitsa pakati pa mapewa ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa