Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 34:20 - Buku Lopatulika

20 Wa fuko la ana a Simeoni, Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Wa fuko la ana a Simeoni, Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 M'fuko la ana a Simeoni akhale Semuele mwana wa Amihudi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Semueli mwana wa Amihudi, wochokera ku fuko la Simeoni;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 34:20
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna nati, Chifukwa anamva Yehova kuti anandida ine, anandipatsa ine mwana wamwamuna uyunso; ndipo anamutcha dzina lake Simeoni.


Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao.


Ndi kumalire a Benjamini, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Simeoni, gawo limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa