Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 34:19 - Buku Lopatulika

19 Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Maina a anthuwo naŵa: M'fuko la Yuda akhale Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 34:19
15 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenganso pakati nabala mwana wamwamuna; nati, Tsopano ndidzamyamikira Yehova; chifukwa chake anamutcha dzina lake Yuda; pamenepo analeka kubala.


Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


ana aamuna a Leya: ndiwo Rubeni mwana woyamba wa Yakobo, ndi Simeoni ndi Levi, ndi Yuda, ndi Zebuloni, ndi Isakara;


Giliyadi ndi wanga, Manasenso ndi wanga; ndipo Efuremu ndi mphamvu ya mutu wanga; Yuda ndiye wolamulira wanga.


Koma Kalebe anatontholetsa anthu pamaso pa Mose, nati, Tikwere ndithu ndi kulilandira lathulathu; popeza tikhozadi kuchita kumene.


Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.


Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.


koma mtumiki wanga Kalebe, popeza anali nao mzimu wina, nanditsata monsemo, ndidzamlowetsa iyeyu m'dziko muja analowamo; ndi mbeu zake zidzakhala nalo.


simudzalowa inu m'dzikolo, ndinakwezapo dzanja langa kukukhalitsani m'mwemo, koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni ndiwo.


Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.


Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, ndiwo a iwo aja adazonda dzikolo, anang'amba zovala zao;


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Muwatengenso akalonga, kalonga mmodzi ku fuko limodzi, agawe dziko likhale cholowa chao.


Koma Kalebe mwana wa Yefune, iye adzaliona; ndidzampatsa iye dziko limene anapondapo, ndi ana ake; popeza analimbika ndi kutsata Yehova.


Za Yuda ndi izi; ndipo anati, Imvani, Yehova, mau a Yuda, ndipo mumfikitse kwa anthu ake; manja ake amfikire; ndipo mukhale inu thandizo lake pa iwo akumuukira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa