Numeri 34:19 - Buku Lopatulika19 Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Maina a anthuwo naŵa: M'fuko la Yuda akhale Kalebe mwana wa Yefune. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda, Onani mutuwo |