Numeri 34:18 - Buku Lopatulika18 Muwatengenso akalonga, kalonga mmodzi ku fuko limodzi, agawe dziko likhale cholowa chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Muwatengenso akalonga, kalonga mmodzi ku fuko limodzi, agawe dziko likhale cholowa chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mutenge mtsogoleri mmodzi pa fuko lililonse, kuti agaŵe dzikolo ngati choloŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Musankhe mtsogoleri mmodzi kuchokera ku fuko lililonse kuti athandize kugawa dzikolo. Onani mutuwo |