Numeri 34:14 - Buku Lopatulika14 popeza fuko la ana a Rubeni monga mwa nyumba za makolo ao, ndi fuko la ana a Gadi monga mwa nyumba za makolo ao, adalandira, ndi hafu la fuko la Manase lalandira cholowa chao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 popeza fuko la ana a Rubeni monga mwa nyumba za makolo ao, ndi fuko la ana a Gadi monga mwa nyumba za makolo ao, adalandira, ndi fuko la hafu la Manase lalandira cholowa chao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Fuko la ana a Rubeni mwa mabanja a makolo ao, ndi fuko la ana a Gadi mwa mabanja a makolo ao, pamodzi ndi theka la fuko la Manase, adalandira kale choloŵa chao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 chifukwa mabanja a fuko la Rubeni, fuko la Gadi, ndi theka la fuko la Manase analandiriratu cholowa chawo. Onani mutuwo |