Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 32:8 - Buku Lopatulika

8 Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Makolo anu adachita zotero, pamene ndidaŵatuma kuchokera ku Kadesi-Baranea, kuti akaone dziko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Izi ndi zimene makolo anu anachita pamene ndinawatuma kuchokera ku Kadesi kukaona dzikolo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ana onse a Israele anadandaulira Mose ndi Aroni; ndi khamu lonse linanena nao, Mwenzi tikadafa m'dziko la Ejipito; kapena mwenzi tikadafa m'chipululu muno!


ndi malire anu adzapinda kuchokera kumwera kunka pokwera Akarabimu, ndi kupitirira ku Zini; ndi kutuluka kwake adzachokera kumwera ku Kadesi-Baranea, nadzatuluka kunka ku Hazara-Adara, ndi kupita kunka ku Azimoni;


Ulendo wake wochokera ku Horebu wofikira ku Kadesi-Baranea, wodzera njira ya phiri la Seiri, ndiwo wa masiku khumi ndi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa