Numeri 32:8 - Buku Lopatulika8 Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Makolo anu adachita zotero, pamene ndidaŵatuma kuchokera ku Kadesi-Baranea, kuti akaone dziko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Izi ndi zimene makolo anu anachita pamene ndinawatuma kuchokera ku Kadesi kukaona dzikolo. Onani mutuwo |