Numeri 3:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo owerengedwa ao, powerenga amuna onse, kuyambira a mwezi umodzi ndi mphambu, ndiwo zikwi zisanu ndi chimodzi kudza mazana awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo owerengedwa ao, powerenga amuna onse, kuyambira a mwezi umodzi ndi mphambu, ndiwo zikwi zisanu ndi chimodzi kudza mazana awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Chiŵerengero chao potsata kuchuluka kwa amuna onse, kuyambira mwana wamwamuna wa mwezi umodzi ndi wopitirirapo, chinali 6,200. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Chiwerengero cha amuna onse kuyambira a mwezi umodzi kapena kupitirirapo chinali 6,200. Onani mutuwo |