Numeri 3:33 - Buku Lopatulika33 Banja la Amali, ndi banja la Amusi ndiwo Amerari; ndiwo mabanja a Merari. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Banja la Amali, ndi banja la Amusi ndiwo a Merari; ndiwo mabanja a Merari. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Amali ndi Amusi anali mabanja otuluka mwa Merari. Ameneŵa ndiwo amene anali mabanja a Merari. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Kwa Merari kunali banja la Mali ndi banja la Musi. Amenewa ndiye anali mabanja a Amerari. Onani mutuwo |