Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:7 - Buku Lopatulika

7 Iwo ndiwo mabanja a Arubeni; owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zitatu kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Iwo ndiwo mabanja a Arubeni; owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zitatu kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ameneŵa, anthu okwanira 43,730, ndiwo anali a m'mabanja a Rubeni, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Awa anali mafuko a Rubeni: onse amene anawerengedwa analipo 43,730.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:7
7 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Rubeni: Hanoki, ndi Palu, ndi Hezironi, ndi Karimi.


owerengedwa ao a fuko la Rubeni, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu ndi chimodzi kudza mazana asanu.


Ndi khamu lake, ndi olembedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu ndi chimodzi kudza mazana asanu.


Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,


Ndipo ana a Perezi ndiwo: Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Hamuli, ndiye kholo la banja la Ahamuli.


Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Karimi, ndiye kholo la banja la Akarimi.


Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa