Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:8 - Buku Lopatulika

8 Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mwana wa Palu anali Eliyabu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mwana wa Palu anali Eliabu,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:8
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Rubeni: Hanoki, ndi Palu, ndi Hezironi, ndi Karimi.


Iwo ndiwo mabanja a Arubeni; owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zitatu kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.


Ndi ana a Eliyabu: Nemuwele, ndi Datani ndi Abiramu. Iwo ndiwo Datani ndi Abiramu omwe aja oitanidwa a khamu, amene anatsutsana ndi Mose ndi Aroni mu msonkhano wa Kora, muja anatsutsana ndi Yehova;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa