Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 26:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mwana wa Palu anali Eliabu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mwana wa Palu anali Eliyabu,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:8
3 Mawu Ofanana  

Ana aamuna a Rubeni ndi awa: Hanoki, Palu, Hezironi ndi Karimi.


Awa anali mafuko a Rubeni: onse amene anawerengedwa analipo 43,730.


ndipo ana a Eliabu anali Nemueli, Datani ndi Abiramu. Datani ndi Abiramu anali gulu la akuluakulu aja amene anawukira Mose ndi Aaroni ndipo analinso mʼgulu la otsatira Kora pamene anawukira Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa