Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:6 - Buku Lopatulika

6 Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Karimi, ndiye kholo la banja la Akarimi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Karimi, ndiye kholo la banja la Akarimi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Hezironi anali kholo la banja la Ahezironi. Karimi anali kholo la banja la Akarimi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 kuchokera mwa Hezironi, fuko la Ahezironi; kuchokera mwa Karimi, fuko la Akarimi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:6
5 Mawu Ofanana  

mphindi yakupha ndi mphindi yakuchiza; mphindi yakupasula ndi mphindi yakumanga;


Koma makanda anu, amene munanena za iwowa kuti adzakhala chakudya, amenewo ndidzawalowetsa, ndipo adzadziwa dzikolo mudalikana.


Ndipo ana a Perezi ndiwo: Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Hamuli, ndiye kholo la banja la Ahamuli.


Rubeni, ndiye woyamba kubadwa wa Israele; ana aamuna a Rubeni ndiwo: Hanoki, ndiye kholo la banja la Ahanoki; Palu, ndiye kholo la banja la Apalu;


Iwo ndiwo mabanja a Arubeni; owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zitatu kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa