Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:57 - Buku Lopatulika

57 Ndipo awa ndi owerengedwa ao a Alevi monga mwa mabanja ao: Geresoni, ndiye kholo la banja la Ageresoni; Kohati, ndiye kholo la banja la Akohati; Merari, ndiye kholo la banja la Amerari.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ndipo awa ndi owerengedwa ao a Alevi monga mwa mabanja ao: Geresoni, ndiye kholo la banja la Ageresoni; Kohati, ndiye kholo la banja la Akohati; Merari, ndiye kholo la banja la Amerari.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Potsata mabanja ao chiŵerengero cha Alevi chinali motere: Geresoni anali kholo la banja la Ageresoni. Kohati anali kholo la banja la Akohati. Merari anali kholo la banja la Amerari.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Alevi omwe anawerengedwa monga mwa mafuko awo ndi awa: kuchokera mwa Geresoni, fuko la Ageresoni; kuchokera mwa Kohati, fuko la Akohati; kuchokera mwa Merari, fuko la Amerari.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:57
12 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ana a Levi: Geresomo, Kohati, ndi Merari.


Ndipo Eleazara mwana wa Aroni anadzitengera mkazi wa ana aakazi a Putiyele akhale mkazi wake, ndipo anambalira Finehasi. Amenewo ndi akulu a makolo a Alevi mwa mabanja ao.


Koma Alevi monga mwa fuko la makolo ao sanawerengedwe mwa iwo.


Koma sanawerenge Alevi mwa ana a Israele; monga Yehova adauza Mose.


Agawire ochuluka ndi ochepa cholowa chao monga mwa kuchita maere.


Werenga ana a Levi monga mwa nyumba ya makolo ao, monga mwa mabanja ao; uwawerenge mwamuna yense wa mwezi umodzi ndi mphambu.


Ndipo ana a Levi maina ao ndi awa: Geresoni, ndi Kohati ndi Merari.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa