Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:56 - Buku Lopatulika

56 Agawire ochuluka ndi ochepa cholowa chao monga mwa kuchita maere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Agawire ochuluka ndi ochepa cholowa chao monga mwa kuchita maere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Choloŵa chaocho, uchigaŵe pakati pa fuko lalikulu ndi laling'ono mwamaere.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Cholowa chawo uchigawe pakati pa fuko lalikulu ndi lalingʼono mwa maere.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:56
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kudzachitika kuti muligawe ndi kuchita maere, likhale cholowa chanu, ndi cha alendo akukhala pakati pa inu; ndipo akhale kwa inu ngati obadwa m'dziko mwa ana a Israele, alandire cholowa pamodzi ndi inu mwa mafuko a Israele.


Koma aligawe ndi kuchita maere; cholowa chao chikhale monga mwa maina a mafuko a makolo ao.


Ndipo awa ndi owerengedwa ao a Alevi monga mwa mabanja ao: Geresoni, ndiye kholo la banja la Ageresoni; Kohati, ndiye kholo la banja la Akohati; Merari, ndiye kholo la banja la Amerari.


Ndipo chiyani tsono? Ichi chimene Israele afunafuna sanachipeze; koma osankhidwawo anachipeza, ndipo otsalawo anaumitsidwa mtima;


Ndipo pali mphatso zosiyana, koma Mzimu yemweyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa