Numeri 26:55 - Buku Lopatulika55 Koma aligawe ndi kuchita maere; cholowa chao chikhale monga mwa maina a mafuko a makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201455 Koma aligawe ndi kuchita maere; cholowa chao chikhale monga mwa maina a mafuko a makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa55 Koma dzikolo uligaŵe mwamaere. Alandire choloŵa chao potsata kuchuluka kwa maina a mafuko a makolo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero55 Dzikolo uligawe pochita maere. Alandire cholowa chawocho potsata mayina a mafuko a makolo awo. Onani mutuwo |