Numeri 26:23 - Buku Lopatulika23 Ana aamuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ana amuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Potsata mabanja ao ana aamuna a Isakara anali aŵa: Tola anali kholo la banja la Atola. Puva anali kholo la banja la Apuva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Zidzukulu za Isakara monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Tola, fuko la Atola; kuchokera mwa Puwa, fuko la Apuwa; Onani mutuwo |