Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 26:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Zidzukulu za Isakara monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Tola, fuko la Atola; kuchokera mwa Puwa, fuko la Apuwa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

23 Ana aamuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ana amuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Potsata mabanja ao ana aamuna a Isakara anali aŵa: Tola anali kholo la banja la Atola. Puva anali kholo la banja la Apuva.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:23
6 Mawu Ofanana  

Ana aamuna a Isakara ndi awa: Tola, Puwa, Yobi ndi Simironi.


Ana a Isakara anali awa: Tola, Puwa, Yasubu ndi Simironi ndipo onse analipo anayi.


Kuchokera mwa zidzukulu za Isakara: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.


Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.


kuchokera mwa Yasubu, fuko la Ayasubu. Kuchokera mwa Simironi, fuko la Asimironi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa