Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:22 - Buku Lopatulika

22 Iwo ndiwo mabanja a Yuda monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu ndi chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Iwo ndiwo mabanja a Yuda monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu ndi chimodzi kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ameneŵa, anthu okwanira 76,500, ndiwo anali a m'mabanja a Yuda, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Awa ndiwo anali mafuko a Yuda. Amene anawerenga analipo 76,500.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:22
7 Mawu Ofanana  

Yuda, abale ako adzakuyamika iwe; dzanja lako lidzakhala pa khosi la adani ako; ana aamuna a atate wako adzakuweramira.


Pakuti Yuda anakula mphamvu mwa abale ake, ndi mtsogoleri anafuma kwa iyeyu, koma ukulu ngwa Yosefe);


Yehova akuonjezereni dalitso, inu ndi ana anu.


Ndipo ana a Perezi ndiwo: Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Hamuli, ndiye kholo la banja la Ahamuli.


Pakuti kwadziwikadi kuti Ambuye wathu anatuluka mwa Yuda; za fuko ili Mose sanalankhule kanthu ka ansembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa