Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:24 - Buku Lopatulika

24 Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Yasubu anali kholo la banja la Ayasubu. Simeoni anali kholo la banja la Asimeoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 kuchokera mwa Yasubu, fuko la Ayasubu. Kuchokera mwa Simironi, fuko la Asimironi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:24
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi.


Ana aamuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni;


Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa