Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:25 - Buku Lopatulika

25 Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Ameneŵa, anthu okwanira 64,300, ndiwo anali a m'mabanja a Isakara, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Awa ndi amene anali a fuko la Isakara. Amene anawerengedwa analipo 64,300.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:25
3 Mawu Ofanana  

Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa