Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:13 - Buku Lopatulika

13 Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Zera anali kholo la banja la Azera. Shaulo anali kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera; kuchokera mwa Sauli, fuko la Asauli.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:13
6 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani.


Wachisanu ndi chitatu wa mwezi wachisanu ndi chitatu ndiye Sibekai Muhusa wa Azera; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Wakhumi wa mwezi wakhumi ndiye Maharai Mnetofa wa Azera; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Ana aamuna a Simeoni monga mwa mabanja ao ndiwo: Nemuwele, ndiye kholo la banja la Anemuwele; Yamini, ndiye kholo la banja la Ayamini; Yakini, ndiye kholo la banja la Ayakini;


Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.


nayandikizitsa zibale za Yuda, nagwira chibale cha Azera; nayandikizitsa chibale cha Azera, mmodzimmodzi, nagwidwa Zabidi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa