Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 26:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera; kuchokera mwa Sauli, fuko la Asauli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

13 Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Zera anali kholo la banja la Azera. Shaulo anali kholo la banja la Ashaulo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:13
6 Mawu Ofanana  

Ana aamuna a Simeoni ndi awa: Yemueli, Yamini, Ohadi, Yakini, Zohari ndi Shaulo amene mayi wake anali wa ku Kanaani.


Wa 8 pa mwezi wa 8 anali Sibekai Mhusati, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000


Wa khumi pa mwezi wa khumi anali Mahazayi wa ku Netofa, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.


Zidzukulu za Simeoni mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Nemueli, fuko la Anemuele; kuchokera mwa Yamini, fuko la Ayamini; kuchokera mwa Yakini fuko la Ayakini;


Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200.


Anabweretsa poyera mbumba zonse za fuko la Yuda, ndipo mbumba ya Zera inagwidwa. Kenaka anatulutsa poyera mabanja onse a mbumba ya Zera ndipo banja la Zabidi linagwidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa