Numeri 26:14 - Buku Lopatulika14 Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ameneŵa, anthu okwanira 22,200, ndiwo a m'mabanja a Simeoni, amene adaŵerengedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200. Onani mutuwo |