Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:14 - Buku Lopatulika

14 Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ameneŵa, anthu okwanira 22,200, ndiwo a m'mabanja a Simeoni, amene adaŵerengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:14
6 Mawu Ofanana  

Koma dzina la Mwisraele adamuphayo, ndiye amene adamupha pamodzi ndi mkazi Mmidiyani, ndiye Zimiri mwana wa Salu, mfumu ya nyumba ya makolo mwa Asimeoni.


Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Shaulo, ndiye kholo la banja la Ashaulo.


Ana aamuna a Gadi monga mwa mabanja ao ndiwo: Zefoni, ndiye kholo la banja la Azefoni; Hagi, ndiye kholo la banja la Ahagi; Suni, ndiye kholo la banja la Suni;


Mwa fuko la Simeoni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko Levi zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Isakara zikwi khumi ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa