Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 24:5 - Buku Lopatulika

5 Ha? Mahema ako ngokoma, Yakobo; zokhalamo zako, Israele!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ha? Mahema ako ngokoma, Yakobo; zokhalamo zako, Israele!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mahema ako, iwe Yakobe, nyumba zako, iwe Israele, si kukoma kwake!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 “Matenti ako ndi okongola kwambiri iwe Yakobo, misasa yako, iwe Israeli!

Onani mutuwo Koperani




Numeri 24:5
13 Mawu Ofanana  

popeza sanawachingamire ana a Israele ndi chakudya ndi madzi, koma anawalemberera Balamu awatemberere; koma Mulungu wathu anasanduliza tembererolo likhale mdalitso.


Moyo wanga ulakalaka, inde ukomokanso ndi kufuna mabwalo a Yehova; mtima wanga ndi thupi langa zifuulira kwa Mulungu wamoyo.


Ichi ndi chiwerengo cha zinthu za chihema, chihema cha mboni, monga anaziwerenga, monga mwa mau a Mose, achite nazo Alevi; anaziwerenga Itamara, mwana wa Aroni wansembe.


Wakongola monsemonse, wokondedwa wanga, namwaliwe, mulibe chilema mwa iwe.


Wakongola, bwenzi langa, namwaliwe ngati Tiriza, wokoma ngati Yerusalemu, woopsa ngati nkhondo ndi mbendera.


Mukhale m'misasa masiku asanu ndi awiri; onse obadwa m'dziko la Israele akhale m'misasa;


Yehova adzalikha munthu wakuchita ichi, wogalamutsa ndi wovomereza m'mahema a Yakobo, ndi iye wopereka chopereka kwa Yehova wa makamu.


Ndipo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose, momwemo anamanga mahema ao pa mbendera zao, momwemonso anayenda paulendo, yense monga mwa mabanja ake, monga mwa nyumba za makolo ake.


Ndipo Balamu anakweza maso ake, naona Israele alikukhala monga mwa mafuko ao; ndipo mzimu wa Mulungu unadza pa iye.


wakumva mau a Mulungu anenetsa, wakuona masomphenya a Wamphamvuyonse, wakugwa pansi maso ake openyuka.


Ziyalika monga zigwa, monga minda m'mphepete mwa nyanja, monga khonje wooka Yehova, monga mikungudza m'mphepete mwa madzi.


Wodala iwe, Israele; akunga iwe ndani, mtundu wa anthu opulumutsidwa ndi Yehova, ndiye chikopa cha thandizo lako, Iye amene akhala lupanga la ukulu wako! Ndi adani ako adzakugonjera; ndipo udzaponda pa misanje yao.


koma sindinafuna kumvera Balamu, potero anakudalitsani chidalitsire, ndipo ndinakulanditsani m'dzanja lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa