Numeri 24:4 - Buku Lopatulika4 wakumva mau a Mulungu anenetsa, wakuona masomphenya a Wamphamvuyonse, wakugwa pansi maso ake openyuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 anenetsa wakumva mau a Mulungu, wakuona masomphenya a Wamphamvuyonse, wakugwa pansi maso ake openyuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 munthu amene akumva mau a Mulungu, munthu amene akuwona Mphambe m'masomphenya, munthu amene akugwa pansi, koma maso ali chipenyere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 uthenga wa amene amamva mawu a Mulungu, yemwe amaona masomphenya wochokera kwa Wamphamvuzonse, yemwe amagwa chafufumimba, koma maso ake ali chipenyere: Onani mutuwo |