Numeri 24:6 - Buku Lopatulika6 Ziyalika monga zigwa, monga minda m'mphepete mwa nyanja, monga khonje wooka Yehova, monga mikungudza m'mphepete mwa madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ziyalika monga zigwa, monga minda m'mphepete mwa nyanja, monga khonje wooka Yehova, monga mikungudza m'mphepete mwa madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Anthu ako ali ngati zigwa zofika patali, ali ngati minda ya m'mbali mwa mtsinje, ali ngati khonje amene Chauta adabzala, ali ngati mitengo ya mkungudza yomera m'mbali mwa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Monga zigwa zotambalala, monga minda mʼmbali mwa mtsinje, monga aloe wodzalidwa ndi Yehova, monga mikungudza mʼmbali mwa madzi. Onani mutuwo |