Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 22:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israele anachitira Aamori.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israele anachitira Aamori.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Balaki mwana wa Zipora adaona zonse zimene Aisraele adachita Aamori.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Tsono Balaki mwana wa Zipori anaona zonse zimene Aisraeli anachitira Aamori,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 22:2
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anamvera mau a Israele, napereka Akanani; ndipo anawaononga konse ndi mizinda yao yomwe; natcha dzina lake la malowo Horoma.


Pamenepo Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu, anauka naponyana ndi Israele; natuma naitana Balamu mwana wa Beori atemberere inu;


Ndipo tsopano kodi inu ndinu wabwino woposa Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu; anatengana konse ndi Israele iyeyu kodi, kapena kuchita nao nkhondo konse kodi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa