Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 21:12 - Buku Lopatulika

12 Pochokapo anayenda ulendo, namanga mahema m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pochokapo anayenda ulendo, namanga mahema m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Atachoka kumeneko, adakamanga m'chigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Kuchoka kumeneko anayendabe nakamanga misasa yawo mʼchigwa cha Zeredi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 21:12
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.


Nachokera ku Iyimu, nayenda namanga mu Diboni Gadi.


Uka, yenda ulendo wako, ndi kuoloka mtsinje wa Arinoni; taonani, ndapereka Sihoni mfumu ya Hesiboni, Mwamori, ndi dziko lake m'dzanja lako; yamba kulilandira, ndi kuutsana naye nkhondo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa