Numeri 21:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo adachoka ku Oboti nakamanga ku Iyeabarimu m'chipululu choyang'anana ndi Mowabu, kuvuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kenaka anasamuka ku Oboti nakamanga misasa yawo ku Iye-Abarimu, mʼchipululu chimene chili kummawa kwa Mowabu, kotulukira dzuwa. Onani mutuwo |