Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:9 - Buku Lopatulika

9 Owerengedwa onse a chigono cha Yuda ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi mphambu mazana anai, monga mwa makamu ao. Ndiwo azitsogolera ulendo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Owerengedwa onse a chigono cha Yuda ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi mphambu mazana anai, monga mwa makamu ao. Ndiwo azitsogolera ulendo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Gulu lonse lathunthu la ku zithando za Yuda, poŵerenga magulu atatu onseŵa, ndi 186,400. Iwowo azikhala patsogolo poyenda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Anthu onse aamuna mʼmisasa ya Yuda, chiwerengero chawo ndi 186,400 monga mwa magulu awo. Iwowo ndiwo aziyamba kusamuka.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:9
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa