Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:8 - Buku Lopatulika

8 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 ndipo ankhondo ake ngokwanira 57,400.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 57,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:8
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Zebuloni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.


Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni.


Owerengedwa onse a chigono cha Yuda ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi mphambu mazana anai, monga mwa makamu ao. Ndiwo azitsogolera ulendo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa