Numeri 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono pabwere fuko la Zebuloni, limene mtsogoleri wake ndi Eliyabu mwana wa Heloni, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni. Onani mutuwo |