Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 ndipo ankhondo ake ngokwanira 54,400.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 54,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:6
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Isakara, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Isakara; ndipo kalonga wa ana a Isakara ndiye Netanele mwana wa Zuwara.


Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni.


Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa