Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 54,400.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 ndipo ankhondo ake ngokwanira 54,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:6
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Isakara chinali 54,400.


Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.


Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.


Awa ndi amene anali a fuko la Isakara. Amene anawerengedwa analipo 64,300.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa